Ahebri 10:13 - Buku Lopatulika13 kuyambira pomwepo alindirira, kufikira adani ake aikidwa akhale mpando kumapazi ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 kuyambira pomwepo alindirira, kufikira adani ake aikidwa akhale mpando kumapazi ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Kumeneko akudikira tsono kuti Mulungu asandutse adani ake kukhala ngati chopondapo mapazi ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Kumeneko akudikira tsono kuti Mulungu asandutse adani ake kukhala chopondapo mapazi ake. Onani mutuwo |