Ahebri 10:10 - Buku Lopatulika10 Ndi chifuniro chimenecho tayeretsedwa mwa chopereka cha thupi la Yesu Khristu, kamodzi, kwatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndi chifuniro chimenecho tayeretsedwa mwa chopereka cha thupi la Yesu Khristu, kamodzi, kwatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Chifukwa chakuti Yesu Khristu adachita zimene Mulungu adaafuna kuti achite, ife tidayeretsedwa ndi nsembe ya thupi lake, limene Iye adapereka kamodzi kokhako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Chifukwa chakuti Yesu Khristu anachita zimene Mulungu anafuna kuti achite, ndife oyeretsedwa ndi nsembe ya thupi lake, limene analipereka kamodzi kokha. Onani mutuwo |