Ahebri 1:11 - Buku Lopatulika11 Iyo idzataika; komatu mukhalitsa; ndipo iyo yonse idzasuka monga malaya; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Iyo idzataika; komatu mukhalitsa; ndipo iyo yonse idzasuka monga malaya; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Zimenezi zidzatha, koma Inu ndinu achikhalire. Zonsezi zidzafwifwa ngati chovala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Zimenezi zidzatha, koma Inu ndinu wachikhalire. Izo zidzatha ngati zovala. Onani mutuwo |