Ahebri 1:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo, Inu, Ambuye, pachiyambipo munaika maziko ake a dziko, ndipo miyamba ili ntchito ya manja anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo, Inu, Ambuye, pachiyambipo munaika maziko ake a dziko, ndipo miyamba ili ntchito ya manja anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Adatinso, “Inu Ambuye, ndinu amene mudalenga dziko lapansi pachiyambi pomwe, zakumwambaku ndi ntchito ya manja anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Mulungu akutinso, “Ambuye, pachiyambi Inu munayika maziko a dziko lapansi; ndipo zakumwambako ndi ntchito za manja anu. Onani mutuwo |