Afilipi 4:11 - Buku Lopatulika11 Si kuti ndinena monga mwa chiperewero, pakuti ndaphunzira ine, kuti zindikwanire zilizonse ndili nazo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Si kuti ndinena monga mwa chiperewero, pakuti ndaphunzira ine, kuti zindikwanire zilizonse ndili nazo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Sindikunena zimenezi modandaula kuti ndikusoŵa kanthu, pakuti ine ndaphunzira kukhutira ndi zimene ndili nazo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Sindikunena izi chifukwa choti ndikusowa thandizo, poti ine ndaphunzira kukhala wokwaniritsidwa ndi zimene ndili nazo. Onani mutuwo |