Afilipi 3:6 - Buku Lopatulika6 monga mwa changu, wolondalonda Mpingo; monga mwa chilungamo cha m'lamulo wokhala wosalakwa ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 monga mwa changu, wolondalonda Mpingo; monga mwa chilungamo cha m'lamulo wokhala wosalakwa ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndipo changu changa chinali chachikulu, kotero kuti ndinkazunza Mpingo. Kunena za chilungamo chopezeka pakutsata Malamulo, ineyo ndinali wopanda cholakwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Kunena za changu changa, ndinkazunza mpingo. Kunena za chilungamo chopezeka chifukwa chotsata malamulo, ineyo ndinali wopanda cholakwa. Onani mutuwo |