Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Afilipi 3:4 - Buku Lopatulika

4 ndingakhale inenso ndili nako kakukhulupirira m'thupi; ngati wina yense ayesa kukhulupirira m'thupi, makamaka ineyu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 ndingakhale inenso ndili nako kakukhulupirira m'thupi; ngati wina yense ayesa kukhulupirira m'thupi, makamaka ineyu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Komabetu ineyo ndikadatha kudalira miyambo yathupiyi. Ngati alipo wina woganiza kuti ali ndi chifukwa chodalira miyambo yathupi yotere, ineyo ndili ndi chifukwa choposa apo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 ngakhale kuti ineyo ndili ndi zifukwa zokwanira kudalira zinthu za thupizo. Ngati pali winanso amene akuganiza kuti ali ndi zifukwa zokwanira kudalira zinthu za thupi, ineyo ndili ndi zifukwa zoposa pamenepo.

Onani mutuwo Koperani




Afilipi 3:4
4 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake yang'anirani mamvedwe anu; pakuti kudzapatsidwa kwa iye amene ali nacho; ndipo kwa iye amene alibe chidzachotsedwa, chingakhale chija aoneka ngati ali nacho.


Kotero kuti ife sitidziwanso munthu tsopano monga mwa thupi; ndipo ngati tazindikira Khristu monga mwa thupi, koma tsopano sitimzindikiranso motero.


Ife ndife Ayuda pachibadwidwe, ndipo sitili ochimwa a kwa amitundu;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa