Afilipi 3:2 - Buku Lopatulika2 Penyererani agalu, penyererani ochita zoipa, penyererani choduladula; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Penyererani agalu, penyererani ochita zoipa, penyererani choduladula; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Chenjera nawoni ochita zaugalu aja, ndiye kuti ochita zoipa, anthu omangodula thupi chabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Chenjerani ndi agalu amenewa, anthu ochita zoyipa, anthu amene amadula thupi lawo. Onani mutuwo |