Afilipi 2:29 - Buku Lopatulika29 Chifukwa chake mumlandire mwa Ambuye, ndi chimwemwe chonse; nimuchitire ulemu oterewa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Chifukwa chake mumlandire mwa Ambuye, ndi chimwemwe chonse; nimuchitire ulemu oterewa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Mlandireni mwachikhristu ndi chimwemwe chachikulu. Anthu otere muziŵachitira ulemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Mulandireni mwa Ambuye ndi chimwemwe chachikulu, ndipo anthu onga iyeyu muziwachitira ulemu. Onani mutuwo |