Afilipi 2:13 - Buku Lopatulika13 pakuti wakuchita mwa inu kufuna ndi kuchita komwe, chifukwa cha kukoma mtima kwake, ndiye Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 pakuti wakuchita mwa inu kufuna ndi kuchita komwe, chifukwa cha kukoma mtima kwake, ndiye Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Paja Mulungu ndiye amene amagwira ntchito mwa inu, muzifuna ndi kutha kuchita zimene zimkomera Iye. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 pakuti ndi Mulungu amene amagwira ntchito mwa inu kuti mufune ndi kuchita zimene zimamukondweretsa Iyeyo. Onani mutuwo |