Afilipi 1:22 - Buku Lopatulika22 Koma ngati kukhala ndi moyo m'thupi ndiko chipatso cha ntchito yanga, sindizindikiranso chimene ndidzasankha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Koma ngati kukhala ndi moyo m'thupi ndiko chipatso cha ntchito yanga, sindizindikiranso chimene ndidzasankha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Koma ngati kukhalabe moyo kungandipatse mwai woti ndigwire ntchito yoonetsa zipatso, sindidziŵa kaya ndingasankhe chiti. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ngati nditi ndipitirire kukhala ndi moyo mʼthupi ndiye kuti kwa ine ndi kugwira ntchito yopindulitsa. Kodi ndisankhe chiyani? Sindikudziwa. Onani mutuwo |