Aefeso 6:3 - Buku Lopatulika3 kuti kukhale bwino ndi iwe, ndi kuti ukhale wa nthawi yaikulu padziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 kuti kukhale bwino ndi iwe, ndi kuti ukhale wa nthawi yaikulu padziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Lonjezolo likuti, “Ukatero, udzakhala wodala, ndipo moyo wako udzakhala wautali pansi pano.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ngati ulemekeza abambo ako ndi amayi ako, “zinthu zidzakuyendera bwino ndipo udzasangalala ndi moyo wautali pa dziko lapansi.” Onani mutuwo |