Aefeso 5:25 - Buku Lopatulika25 Amuna inu, kondani akazi anu, monganso Khristu anakonda Mpingo, nadzipereka yekha m'malo mwake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Amuna inu, kondani akazi anu, monganso Khristu anakonda Mpingo, nadzipereka yekha m'malo mwake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Inu amuna, muzikonda akazi anu, monga momwe Khristu adakondera Mpingo, nadzipereka chifukwa cha Mpingowo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Inu amuna, kondani akazi anu monga momwe Khristu anakondera mpingo nadzipereka yekha mʼmalo mwa mpingowo Onani mutuwo |