Aefeso 5:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo musaledzere naye vinyo, m'mene muli chitayiko; komatu mudzale naye Mzimu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo musaledzere naye vinyo, m'mene muli chitayiko; komatu mudzale naye Mzimu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Musaledzere vinyo, kumeneko nkudzitaya, koma mudzazidwe ndi Mzimu Woyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Musaledzere ndi vinyo, chifukwa adzawononga moyo wanu. Mʼmalo mwake, mudzazidwe ndi Mzimu Woyera. Onani mutuwo |