Aefeso 5:17 - Buku Lopatulika17 Chifukwa chake musakhale opusa, koma dziwitsani chifuniro cha Ambuye nchiyani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Chifukwa chake musakhale opusa, koma dziwitsani chifuniro cha Ambuye nchiyani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Nchifukwa chake musakhale opusa, koma dziŵani zimene Ambuye afuna kuti muchite. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Choncho musakhale opusa, koma mudziwe zimene Ambuye akufuna kuti muchite. Onani mutuwo |