Aefeso 5:16 - Buku Lopatulika16 akuchita machawi, popeza masiku ali oipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 akuchita machawi, popeza masiku ali oipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Mukhale achangu, osataya nthaŵi yanu pachabe, pakuti masiku ano ngoipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Gwiritsani ntchito mpata uliwonse, chifukwa masiku ano ndi oyipa. Onani mutuwo |