Aefeso 4:6 - Buku Lopatulika6 Mulungu mmodzi ndi Atate wa onse amene ali pamwamba pa onse, ndi mwa onse, ndi m'kati mwa zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Mulungu mmodzi ndi Atate wa onse amene ali pamwamba pa onse, ndi mwa onse, ndi m'kati mwa zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pali Mulungu mmodzi amene ali Atate a anthu onse. Iye ali pamwamba pa onse, amagwira ntchito kudzera mwa onse, ndipo ali mwa onse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mulungu mmodzi ndi Atate a onse, ndipo ali mwa onse. Onani mutuwo |