Aefeso 4:3 - Buku Lopatulika3 ndi kusamalitsa kusunga umodzi wa Mzimu mwa chimangiriro cha mtendere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 ndi kusamalitsa kusunga umodzi wa Mzimu mwa chimangiriro cha mtendere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 ndipo muziyesetsa kusunga umodzi mwa Mzimu Woyera pa kulunzana mu mtendere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Muyesetse kusunga umodzi wa Mzimu; umodzi umene umatimangirira pamodzi mu mtendere. Onani mutuwo |