Aefeso 4:26 - Buku Lopatulika26 Kwiyani, koma musachimwe; dzuwa lisalowe muli chikwiyire, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Kwiyani, koma musachimwe; dzuwa lisalowe muli chikwiyire, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Inde mwina nkupsa mtima, koma musachimwe, ndipo musalole kuti dzuŵa likuloŵereni muli chikwiyire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Kwiyani koma musachimwe. Dzuwa lisalowe mukanali chikwiyire. Onani mutuwo |