Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Aefeso 4:27 - Buku Lopatulika

27 ndiponso musampatse malo mdierekezi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 ndiponso musampatse malo mdierekezi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Musampatse mpata Satana woti akugwetseni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Musamupatse mpata Satana.

Onani mutuwo Koperani




Aefeso 4:27
7 Mawu Ofanana  

Koma Petro anati, Ananiya, Satana anadzaza mtima wako chifukwa ninji kudzanyenga Mzimu Woyera, ndi kupatula pa mtengo wake wa mundawo?


Musabwezere choipa, okondedwa, koma patukani pamkwiyo; pakuti kwalembedwa, Kubwezera kuli kwanga, Ine ndidzabwezera, ati Ambuye.


Tavalani zida zonse za Mulungu, kuti mudzakhoze kuchilimika pokana machenjerero a mdierekezi.


koposa zonse mutadzitengeranso chikopa cha chikhulupiriro, chimene mudzakhoza kuzima nacho mivi yonse yoyaka moto ya woipayo.


Potero mverani Mulungu; koma kanizani mdierekezi, ndipo adzakuthawani inu.


Khalani odzisungira, dikirani; mdani wanu mdierekezi, monga mkango wobuma, ayendayenda ndi kufunafuna wina akamlikwire:


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa