Aefeso 2:18 - Buku Lopatulika18 kuti mwa Iye ife tonse awiri tili nao malowedwe athu kwa Atate, mwa Mzimu mmodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 kuti mwa Iye ife tonse awiri tili nao malowedwe athu kwa Atate, mwa Mzimu mmodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Tsopano kudzera mwa Khristu ife tonse, Ayuda ndi a mitundu ina, tingathe kufika kwa Atate mwa Mzimu Woyera mmodzi yemweyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Pakuti mwa Iye, ife tonse titha kufika kwa Atate mwa Mzimu mmodzi. Onani mutuwo |