Aefeso 2:16 - Buku Lopatulika16 ndi kuti akayanjanitse awiriwa ndi Mulungu, m'thupi limodzi mwa mtandawo, atapha nao udaniwo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 ndi kuti akayanjanitse awiriwa ndi Mulungu, m'thupi limodzi mwa mtandawo, atapha nao udaniwo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Khristu adafa pa mtanda kuti athetse chidani, ndipo kuti mwa mtandawo aphatikize pamodzi m'thupi limodzi mitundu iŵiriyo, ndi kuiyanjanitsa ndi Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 ndi kuyanjanitsa onse awiriwa mʼthupi lake kwa Mulungu, kudzera pa mtanda, umene Iye anaphapo udani wawo. Onani mutuwo |