Aefeso 1:9 - Buku Lopatulika9 Anatizindikiritsa ife chinsinsi cha chifuniro chake, monga kunamkomera ndi monga anatsimikiza mtima kale mwa Iye, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Anatizindikiritsa ife chinsinsi cha chifuniro chake, monga kunamkomera ndi monga anatsimikiza mtima kale mwa Iye, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Mwa luntha ndi nzeru adatiwululira chifuniro chake chimene kale chinali chobisika. Zimene adaati achite mwa kukoma mtima kwake ndi zomwe Iye mwini adaakonzeratu kale. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iye watiwululira chifuniro chake chimene chinali chobisika, chimene anachikonzeratu mwa Khristu, molingana ndi kukoma mtima kwake. Onani mutuwo |