Aefeso 1:10 - Buku Lopatulika10 kuti pa makonzedwe a makwaniridwe a nyengozo, akasonkhanitse pamodzi zonse mwa Khristu, za kumwamba, ndi za padziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 kuti pa makonzedwe a makwaniridwe a nyengozo, akasonkhanitse pamodzi zonse mwa Khristu, za kumwamba, ndi za padziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Chimene Mulungu adalongosola kuti achite itakwana nthaŵi, nchakuti asonkhanitse pamodzi mwa Khristu zinthu zonse za Kumwamba ndi zapansipano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Chimene anakonza kuti chichitike nʼchakuti, ikakwana nthawi yake asonkhanitsa pamodzi mwa Khristu zinthu zonse za kumwamba ndi pa dziko lapansi. Onani mutuwo |