Aefeso 1:15 - Buku Lopatulika15 Mwa ichi inenso, m'mene ndamva za chikhulupiriro cha mwa Ambuye Yesu chili mwa inu ndi chikondi chanu, chimenenso mufikitsira oyera mtima onse, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Mwa ichi inenso, m'mene ndamva za chikhulupiriro cha mwa Ambuye Yesu chili mwa inu ndi chikondi chanu, chimenenso mufikitsira oyera mtima onse, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Ndamva kuti mukukhulupirira Ambuye Yesu, ndiponso kuti mumakonda anthu a Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Choncho, kuyambira pamene ndinamva za chikhulupiriro chanu mwa Ambuye Yesu ndi za chikondi chanu pa oyera mtima onse, Onani mutuwo |