3 Yohane 1:9 - Buku Lopatulika9 Ndalemba kanthu kwa Mpingo; komatu Diotrefe uja, wofuna kukhala wamkulu wa iwo, satilandira ife. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndalemba kanthu kwa Mpingo; komatu Diotrefe uja, wofuna kukhala wamkulu wa iwo, satilandira ife. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndidalembera mpingo mau pang'ono, koma Diotrefe safuna kundimvera. Iye amafuna kukhala mtsogoleri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndinalembera mpingo, koma Diotrefe, amene amafuna kukhala wotsogolera, sanafune kutimvera. Onani mutuwo |