2 Timoteyo 4:4 - Buku Lopatulika4 ndipo adzalubza dala pachoonadi, nadzapatukira kutsata nthano zachabe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 ndipo adzalubza dala pachoonadi, nadzapatukira kutsata nthano zachabe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Adzafulatira choona, osafunanso kuchimva, ndipo adzangotsata nthano chabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Sadzafuna kumva choona koma adzafuna kumva nthano chabe. Onani mutuwo |