2 Timoteyo 2:9 - Buku Lopatulika9 m'menemo ndimva zowawa kufikira zomangira, monga wochita zoipa; koma mau a Mulungu samangika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 m'menemo ndimva zowawa kufikira zomangira, monga wochita zoipa; koma mau a Mulungu samangika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Chifukwa cha Uthenga Wabwinowu ndimamva zoŵaŵa, mpakanso kumangidwa m'ndende, ngati chigaŵenga. Koma mau a Mulungu sangathe kumangidwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 umene ndikuwuvutikira choterewu mpaka kumangidwa ndi maunyolo ngati wakuba. Koma mawu a Mulungu sanamangidwe ndi maunyolo. Onani mutuwo |