2 Timoteyo 2:8 - Buku Lopatulika8 Kumbukira Yesu Khristu, wouka kwa akufa, wochokera m'mbeu ya Davide, monga mwa Uthenga Wabwino wanga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Kumbukira Yesu Khristu, wouka kwa akufa, wochokera m'mbeu ya Davide, monga mwa Uthenga Wabwino wanga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Kumbukira Yesu Khristu amene adauka kwa akufa, ndiponso anali mmodzi mwa zidzukulu za Davide, monga umaphunzitsira Uthenga Wabwino umene ine ndimalalika. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Kumbukira Yesu Khristu wochokera ku mtundu wa Davide kuti anauka kwa akufa. Uwu ndiye uthenga wanga wabwino Onani mutuwo |