2 Timoteyo 2:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo iwe, mwana wanga, limbika m'chisomo cha mwa Khristu Yesu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo iwe, mwana wanga, limbika m'chisomo cha m'Khristu Yesu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsono iwe, mwana wanga, limbika pakugwiritsa ntchito mphatso zaulere zimene uli nazo mwa Khristu Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Tsono iwe, mwana wanga, limbika mʼchisomo chimene chili mwa Khristu Yesu. Onani mutuwo |