2 Timoteyo 1:1 - Buku Lopatulika1 Paulo mtumwi wa Khristu Yesu mwa chifuniro cha Mulungu, monga mwa lonjezano la moyo wa mu Khristu Yesu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Paulo mtumwi wa Khristu Yesu mwa chifuniro cha Mulungu, monga mwa lonjezano la moyo wa m'Khristu Yesu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ndine, Paulo, mtumwi wa Khristu Yesu, mwa kufuna kwa Mulungu. Adandituma kuti ndilalike chilonjezo cha moyo umene uli mwa Khristu Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Paulo mtumwi wa Khristu Yesu mwa chifuniro cha Mulungu. Anandituma kuti ndilalike za lonjezo la moyo umene uli mwa Khristu Yesu. Onani mutuwo |