2 Samueli 8:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo pamene Toi mfumu ya ku Hamati anamva kuti Davide adakantha khamu lonse la Hadadezere, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo pamene Toi mfumu ya ku Hamati anamva kuti Davide adakantha khamu lonse la Hadadezere, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Pamene Toi mfumu ya ku Hamati adamva kuti Davide wagonjetsa gulu lonse lankhondo la Hadadezere, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Tou, mfumu ya Hamati atamva kuti Davide wagonjetsa gulu lonse lankhondo la Hadadezeri, Onani mutuwo |