2 Samueli 7:21 - Buku Lopatulika21 Chifukwa cha mau anu, ndi monga mwa mtima wanu, munachita ukulu wonse umene kuuzindikiritsa mnyamata wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Chifukwa cha mau anu, ndi monga mwa mtima wanu, munachita ukulu wonse umene kuuzindikiritsa mnyamata wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Mwachita zazikulu zonsezi chifukwa cha lonjezo lanu, ndiponso potsata zimene mtima wanu umafuna, kuti mtumiki wanune ndidziŵe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Chifukwa cha mawu anu komanso mwa chifuniro chanu, mwachita chinthu chachikulu ichi ndipo mwachiwulula kwa mtumiki wanu. Onani mutuwo |