2 Samueli 7:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo Davide adzaonjezanso kunenanso ndi Inu? Pakuti mudziwa mnyamata wanu, Yehova Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo Davide adzaonjezanso kunenanso ndi Inu? Pakuti mudziwa mnyamata wanu, Yehova Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 “Nanga ine ndingathe kunena chiyaninso kwa Inu? Paja mumandidziŵa mtumiki wanune, Inu Chauta Wamphamvuzonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Kodi Davide anenenso chiyani kwa Inu? Pakuti Inu Ambuye Wamphamvuzonse mukumudziwa mtumiki wanu. Onani mutuwo |