2 Samueli 7:15 - Buku Lopatulika15 koma chifundo changa sichidzamchokera iye, monga ndinachichotsera Saulo amene ndinamchotsa pamaso pako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 koma chifundo changa sichidzamchokera iye, monga ndinachichotsera Saulo amene ndinamchotsa pamaso pako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Koma sindidzamchotsera chikondi changa chosasinthika, monga m'mene ndidaachitira ndi Saulo, amene ndidamkana, kuti uloŵe ufumu ndiwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Koma sindidzasiya kumukonda, monga ndinachitira ndi Sauli, amene ndinamuchotsa iwe usanakhale mfumu. Onani mutuwo |