Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 4:10 - Buku Lopatulika

10 muja munthu wina anandiuza kuti, Onani Saulo wamwalira, ndi kulingalira kuti alikubwera nao uthenga wabwino, ndinamgwira ndi kumupha ku Zikilagi, ndiyo mphotho yake ndinampatsa chifukwa cha uthenga wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 muja munthu wina anandiuza kuti, Onani Saulo wamwalira, ndi kulingalira kuti alikubwera nao uthenga wabwino, ndinamgwira ndi kumupha ku Zikilagi, ndiyo mphotho yake ndinampatsa chifukwa cha uthenga wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 pamene wina adaandiwuza kuti Saulo wamwalira, naganiza kuti wabwera ndi uthenga wabwino, ine ndidamgwira, ndipo ndidamupha ku Zikilagi. Imeneyo idaali mphotho yomwe adalandira chifukwa cha uthenga wakewo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 pamene munthu wina anandiwuza kuti, ‘Sauli wafa’ ndipo ankaganiza kuti wabweretsa nkhani yabwino, ine ndinamugwira ndi kumupha ku Zikilagi. Iyi inali mphotho imene ndinapereka kwa iyeyo chifukwa cha uthenga wake!

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 4:10
1 Mawu Ofanana  

Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa