2 Samueli 3:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo panali, pokhala nkhondo pakati pa nyumba ya Saulo ndi nyumba ya Davide, Abinere analimbikira nyumba ya Saulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo panali, pokhala nkhondo pakati pa nyumba ya Saulo ndi nyumba ya Davide, Abinere analimbikira nyumba ya Saulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Pamene kunali nkhondo pakati pa anthu a Saulo ndi anthu a Davide, Abinere adayamba kudzipatsa mphamvu pa anthu a Saulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pamene kunali nkhondo pakati pa banja la Sauli ndi banja la Davide, Abineri anayamba kudzipatsa yekha mphamvu pakati pa banja la Sauli. Onani mutuwo |