2 Samueli 3:35 - Buku Lopatulika35 Ndipo anthu onse anadza kudzadyetsa Davide chakudya kukali msana; koma Davide analumbira nati, Mulungu andilange naonjezepo, ngati ndilawa mkate kapena kanthu kena, lisanalowe dzuwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201435 Ndipo anthu onse anadza kudzadyetsa Davide chakudya kukali msana; koma Davide analumbira nati, Mulungu andilange naonjezepo, ngati ndilawa mkate kapena kanthu kena, lisanalowe dzuwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa35 Kenaka anthuwo adadza kudzapempha mfumu kuti adye chakudya kudakali koyera. Koma Davide adalumbira kuti, “Mulungu andilange kwabasi, ngati ndidya chakudya kapena kanthu kena kalikonse dzuŵa lisanaloŵe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero35 Kenaka onse anabwera kwa Davide kumuwumiriza kuti adye kusanade. Koma Davide analumbira kuti, “Mulungu andilange ine, andilange kwambiri, ngati ndilawe buledi kapena chilichonse dzuwa lisanalowe!” Onani mutuwo |