Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 3:32 - Buku Lopatulika

32 Ndipo anaika Abinere ku Hebroni; ndi mfumu inakweza mau ake nilira ku manda a Abinere, nalira anthu onse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Ndipo anaika Abinere ku Hebroni; ndi mfumu inakweza mau ake nilira ku manda a Abinere, nalira anthu onse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Adakamuika Abinere ku Hebroni. Ndiye mfumu idalira mokweza mau ku manda a Abinere. Nawonso anthu onse adalira kwambiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Iwo anamuyika Abineri mʼmanda ku Hebroni ndipo mfumu inalira mokweza pa manda a Abineri. Ndipo anthu onse analiranso.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 3:32
8 Mawu Ofanana  

Nabuma, nalira misozi, nasala kudya kufikira madzulo, chifukwa cha Saulo ndi mwana wake Yonatani, ndi anthu a Yehova, ndi banja la Israele, chifukwa adagwa ndi lupanga.


Ndipo mfumuyo inagwidwa chisoni, nikwera ku chipinda chosanja pa chipatacho, nilira misozi; niyenda, nitero, Mwana wanga Abisalomu, mwana wanga Abisalomu; mwana wanga! Mwenzi nditakufera ine, Abisalomu, mwana wanga, mwana wanga!


Ndipo Davide analamulira anyamata ake, iwo nawapha, nawapachika m'mbali mwa thamanda ku Hebroni atawadula manja ndi mapazi ao. Koma mutu wa Isiboseti anautenga nauika m'manda a Abinere ku Hebroni.


ichinso ndi mphulupulu yoyenera oweruza kunena mlandu wake; pakuti ndikadakana Mulungu ali m'mwamba.


Ngati ndakondwera nalo tsoka la wondida, kapena kudzitukula pompeza choipa;


Usakondwere pakugwa mdani wako; mtima wako usasekere pokhumudwa iye;


Ndipo Davide ndi anthu amene anali naye anakweza mau ao, nalira misozi, kufikira analibe mphamvu yakuliranso.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa