2 Samueli 3:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo anaika Abinere ku Hebroni; ndi mfumu inakweza mau ake nilira ku manda a Abinere, nalira anthu onse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo anaika Abinere ku Hebroni; ndi mfumu inakweza mau ake nilira ku manda a Abinere, nalira anthu onse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Adakamuika Abinere ku Hebroni. Ndiye mfumu idalira mokweza mau ku manda a Abinere. Nawonso anthu onse adalira kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Iwo anamuyika Abineri mʼmanda ku Hebroni ndipo mfumu inalira mokweza pa manda a Abineri. Ndipo anthu onse analiranso. Onani mutuwo |