2 Samueli 24:23 - Buku Lopatulika23 zonsezi, mfumu, Arauna akupatsani mfumu. Ndipo Arauna anati kwa mfumu, Yehova Mulungu wanu akulandireni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 zonsezi, mfumu, Arauna akupatsani mfumu. Ndipo Arauna anati kwa mfumu, Yehova Mulungu wanu akulandireni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Zonsezi Arauna adazipereka kwa mfumu, ndipo adapitiriza nati, “Chauta Mulungu wanu, alandire nsembe zanuzo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Inu mfumu, Arauna akupereka zonsezi kwa inu mfumu.” Arauna anatinso kwa iye, “Yehova Mulungu wanu akuvomerezeni.” Onani mutuwo |