2 Samueli 24:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo pamene mthenga anatambasulira dzanja lake ku Yerusalemu kuuononga, choipacho chinachititsa Yehova chisoni, Iye nauza mthenga wakuononga anthuwo, kuti, Kwafikira tsopano, bweza dzanja lako. Ndipo mthenga wa Yehova anali pa dwale la Arauna Myebusi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo pamene mthenga anatambasulira dzanja lake ku Yerusalemu kuuononga, choipacho chinachititsa Yehova chisoni, Iye nauza mthenga wakuononga anthuwo, kuti, Kwafikira tsopano, bweza dzanja lako. Ndipo mthenga wa Yehova anali pa dwale la Arauna Myebusi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ndipo pamene mngelo adatambalitsa dzanja lake kuloza mzinda wa Yerusalemu kuti auwononge, Chauta adasintha maganizo achilangowo, nauza mngelo wake amene ankaononga anthu uja kuti, “Iyai, basi tsopano! Kwakwanira. Bweza dzanja lakolo.” Nthaŵi imeneyo nkuti mngelo wa Chautayo ataima pa malo opunthira tirigu a Arauna Myebusi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Pamene mngelo anatambasula dzanja lake kuti awononge Yerusalemu, Yehova anamva chisoni chifukwa cha zowawazo ndipo anati kwa mngelo amene ankawononga anthu uja, “Basi kwakwanira! Leka kuwononga.” Nthawi imeneyo mngelo wa Yehova anali atayima pamalo opunthira tirigu a Arauna Myebusi. Onani mutuwo |