Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 23:30 - Buku Lopatulika

30 Benaya Mpiratoni, Hidai wa ku timitsinje ta Gaasi;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Benaya Mpiratoni, Hidai wa ku timitsinje ta Gaasi;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Panalinso Benaya wa ku Piratoni, Hidai wa ku mitsinje ya ku Gaasi,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Benaya Mpiratoni, Hidayi wa ku zigwa za Gaasi.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 23:30
7 Mawu Ofanana  

Wakhumi ndi chimodzi wa mwezi wakhumi ndi chimodzi ndiye Benaya Mpiratoni wa ana a Efuremu; ndi m'chigawo mwake zikwi makumi awiri mphambu zinai.


amenewa anatembenuka nakwera kumapiri nalowa ku chigwa cha Esikolo, nachizonda.


Ndipo anamuika m'malire a cholowa chake mu Timnati-Sera, ndiwo ku mapiri a Efuremu kumpoto kwa phiri la Gaasi.


Ndi pambuyo pake Abidoni mwana wa Hilele wa ku Piratoni anaweruza Israele.


Nafa Abidoni mwana wa Hilele wa ku Piratoni, naikidwa mu Piratoni m'dziko la Efuremu ku mapiri a Amaleke.


Ndipo anamuika m'malire a cholowa chake mu Timnati-Heresi, ku mapiri a Efuremu, kumpoto kwa phiri la Gaasi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa