2 Samueli 21:7 - Buku Lopatulika7 Koma mfumu inaleka Mefiboseti mwana wa Yonatani, mwana wa Saulo, chifukwa cha lumbiro la kwa Yehova linali pakati pa Davide ndi Yonatani mwana wa Saulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Koma mfumu inaleka Mefiboseti mwana wa Yonatani, mwana wa Saulo, chifukwa cha lumbiro la kwa Yehova linali pakati pa Davide ndi Yonatani mwana wa Saulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Koma mfumu idasunga Mefiboseti, mwana wa Yonatani, mwana wa Saulo, chifukwa cha kulumbira kumene mfumu Davideyo ndi Yonatani mwana wa Saulo adaachita pamaso pa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Koma mfumu inasunga Mefiboseti mwana wa Yonatani, mwana wa Sauli, chifukwa cha kulumbira kumene mfumu Davide ndi Yonatani mwana wa Sauli anachita pamaso pa Yehova. Onani mutuwo |