2 Samueli 21:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo m'masiku a Davide munali njala, zaka zitatu; ndipo Davide anafunsira kwa Yehova. Ndipo Yehova anati, Ndicho chifukwa cha Saulo ndi nyumba yake yamwazi, popeza iye anawapha Agibiyoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo m'masiku a Davide munali njala, zaka zitatu; ndipo Davide anafunsira kwa Yehova. Ndipo Yehova anati, Ndicho chifukwa cha Saulo ndi nyumba yake yamwazi, popeza iye anawapha Agibiyoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Nthaŵi ya ufumu wa Davide kunali njala ya zaka zitatu motsatanatsatana. Ndiye Davide adapempha nzeru kwa Chauta, ndipo Chauta adamuuza kuti, “Saulo ndi banja lake adakali nawobe mlandu uja wopha Agibiyoniwu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Pa nthawi ya ulamuliro wa Davide kunali njala kwa zaka zitatu zotsatana. Kotero Davide anapemphera kwa Yehova. Yehova anati, “Izi zachitika chifukwa chakuti Sauli ndi banja lake akanali ndi mlandu wakupha Agibiyoni.” Onani mutuwo |