Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Samueli 20:26 - Buku Lopatulika

26 ndiponso Ira Myairi anali ansembe a Davide.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 ndiponso Ira Myairi anali ansembe a Davide.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Ndipo Ira Myairi nayenso anali wansembe wa Davide.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 ndipo Ira wa ku Yairi anali wansembe wa Davide.

Onani mutuwo Koperani




2 Samueli 20:26
14 Mawu Ofanana  

ndipo anamkweza iye m'galeta wake wachiwiri amene anali naye: ndipo anafuula patsogolo pa iye, Gwadani; ndipo anamkhazika iye wolamulira dziko lonse la Ejipito.


Ndipo Farao anamutcha dzina la Yosefe Zafenati-Panea; ndipo anampatsa akwatire Asenati mwana wamkazi wa Potifera wansembe wa Oni. Ndipo Yosefe anatuluka wolamulira, nayendayenda m'dziko la Ejipito.


ndi Seva anali mlembi; ndi Zadoki ndi Abiyatara anali ansembe;


Ndipo m'masiku a Davide munali njala, zaka zitatu; ndipo Davide anafunsira kwa Yehova. Ndipo Yehova anati, Ndicho chifukwa cha Saulo ndi nyumba yake yamwazi, popeza iye anawapha Agibiyoni.


Ira Mwitiri, Garebu Mwitiri;


Ndipo Benaya mwana wa Yehoyada anayang'anira Akereti ndi Apeleti. Ndipo ana a Davide anali ansembe ake.


ndi Azariya mwana wa Natani anayang'anira akapitao, ndipo Zabudi mwana wa Natani anali wansembe ndi nduna yopangira mfumu,


Ira Mwitiri, Garebu Mwitiri,


Ndi oimbira, ana a Asafu, anali pokhala pao, monga adalamulira Davide, ndi Asafu, ndi Hemani, ndi Yedutuni mlauli wa mfumu; ndi olindirira anali pa zipata zonse, analibe kuleka utumiki wao; pakuti abale ao Alevi anawakonzera.


Koma anati, Wakuika iwe ndani ukhale mkulu ndi woweruza wathu? Kuteroku ukuti undiphe, monga unamupha Mwejipito? Ndipo Mose anachita mantha, nanena, Ndithu chinthuchi chadziwika.


Ndipo wansembe wa Midiyani anali nao ana aakazi asanu ndi awiri, amene anadza kudzatunga madzi; ndipo anadzaza mimwero kuti amwetse gulu la atate wao.


Koma sanatulutse dzanja lake pa akulu a ena a Israele; ndipo anapenya Mulungu, nadya, namwa.


Yairi mwana wa Manase analanda dziko lonse la Arigobu, kufikira malire a Agesuri ndi Amaakati; nalitcha dzina lake, Basani Havoti-Yairi, kufikira lero lino).


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa