2 Samueli 20:24 - Buku Lopatulika24 ndi Adoramu anayang'anira msonkho; ndi Yehosafati mwana wa Ahiludi anali wolemba mbiri; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 ndi Adoramu anayang'anira msonkho; ndi Yehosafati mwana wa Ahiludi anali wolemba mbiri; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Adoniramu anali mkulu woyang'anira za thangata. Yehosafati, mwana wa Ahiludi, anali mlembi wolemba mbiri ya dziko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Adoramu amayangʼanira anthu ogwira ntchito ya thangata, Yehosafati mwana wa Ahiludi anali mlembi wa zochitika, Onani mutuwo |