2 Samueli 2:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo tsopano Yehova achitire inu chokoma ndi choonadi; inenso ndidzakubwezerani chokoma ichi, popeza munachita chinthuchi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo tsopano Yehova achitire inu chokoma ndi choonadi; inenso ndidzakubwezerani chokoma ichi, popeza munachita chinthuchi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsopano Chauta akuwonetseni chikondi chake chosasinthika, ndiponso kukhulupirika kwake kwa inu. Ndipotu inenso ndidzakuchitirani zabwino chifukwa cha zimene mwachitazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Tsopano Yehova akuonetseni kukoma mtima ndi kukhulupirika kwake ndipo inenso ndidzakukomerani mtima chifukwa munachita zimenezi. Onani mutuwo |