2 Samueli 2:5 - Buku Lopatulika5 Pamenepo Davide anatumiza mithenga kwa anthu a ku Yabesi-Giliyadi, nanena nao, Mudalitsike ndi Yehova inu, popeza munachitira chokoma ichi mbuye wanu Saulo, ndi kumuika. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pamenepo Davide anatumiza mithenga kwa anthu a ku Yabesi-Giliyadi, nanena nao, Mudalitsike ndi Yehova inu, popeza munachitira chokoma ichi mbuye wanu Saulo, ndi kumuika. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 adatuma amithenga kwa anthuwo kukaŵauza kuti, “Chauta akudalitseni, poti mudaonetsa kukhulupirika kwanu pomuika Saulo mbuyanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 iye anatuma amithenga kwa anthu a ku Yabesi Giliyadi kuti akayankhule nawo kuti, “Yehova akudalitseni poonetsa kukoma mtima kwanu kwa Sauli mbuye wanu pomuyika mʼmanda. Onani mutuwo |