2 Samueli 2:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo ana a Benjamini anaunjikana pamodzi kutsata Abinere, nakhala gulu limodzi, naima pamwamba pa chitunda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo ana a Benjamini anaunjikana pamodzi kutsata Abinere, nakhala gulu limodzi, naima pamwamba pa chitunda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Abenjamini adasonkhana pamodzi kuthandiza Abinere, ndipo adapanga gulu limodzi lankhondo, nakaima pamwamba pa phiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Pamenepo anthu a fuko la Benjamini anasonkhana kudzathandiza Abineri. Iwo anapanga gulu ndipo anayima pamwamba pa phiri. Onani mutuwo |