2 Samueli 2:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo Abinere ananena ndi Yowabu, Aimirire anyamata nasewere pamaso pathu. Nati Yowabu, Aimirire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo Abinere ananena ndi Yowabu, Aimirire anyamata nasewere pamaso pathu. Nati Yowabu, Aimirire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Abinere adauza Yowabu kuti, “Anyamata anu ndi athu abwere, amenyane tiwone.” Yowabu adati, “Chabwino, namenyane.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Kenaka Abineri anati kwa Yowabu, “Tiye tibweretse ena mwa anyamata athu kuti amenyane patsogolo pathupa.” Yowabu anayankha, “Chabwino, amenyane.” Onani mutuwo |